Music Video

Praise Umali - Plan Feat Gwamba (Official Video)
Watch Praise Umali - Plan Feat  Gwamba (Official Video) on YouTube

Featured In

Credits

COMPOSITION & LYRICS
Praise Umali
Praise Umali
Songwriter
Duncan Zgambo
Duncan Zgambo
Songwriter

Lyrics

I worried all the time
I thought I'm running out of time
Can't take it a day at a time sometimes
Man our dreams have been too loud since
We were only young kids
And now, we grown they loud still
I know ndizambiri umafuna mtima
Nde pena mantha ankadzandigwila
Like what if we don't make it (yeah yeah)
What if we don't make it (yeah yeah)
Koma tachoka nkutali
Mulungu anali ndi pulani
Pulani
Inu Zonse ndi nthawi
Mulungu anali ndi pulani
Pulani
Yopanga za ifeyo (oooh oooh oooh)
Yopanga za ifeyo
Akupanga za ifeyo (oooh oooh oooh)
Akupanga za ifeyo
Yoh
Venue yomweyo ena amaflopa
Samatrenda nyimbo zawo akadropa
Nde pena pride imafuna idzindikopa
Koma mbuye wanga sangakondwe kuti nzizipopa
Nde rule number 1, kumakhala humble
Poti ukazikweza amasiya kupanga zako
Rule number 2, osakhala ndi tsankho
Poti lero ndi kape mawa ali pamwamba pako
Nkayang'ana kumbuyo ngati ndingokuwa mbuye
Ndinakhonza chani kuti inu mundimasule
Mwandichotsa kutali kwinakunso Mulambule
Ulendowu ndiwautali koma
Koma tachoka nkutali
Mulungu anali ndi pulani
Pulani
Inu Zonse ndi nthawi
Mulungu anali ndi pulani
Pulani
Yopanga za ifeyo (oooh oooh oooh)
Yopanga za ifeyo
Akupanga za ifeyo (oooh oooh oooh)
Akupanga za ifeyo
Written by: Duncan Zgambo, Praise Umali
instagramSharePathic_arrow_out