Music Video

Featured In

Credits

PERFORMING ARTISTS
Tboy Tanonga
Tboy Tanonga
Performer
COMPOSITION & LYRICS
Tanonga Nswana
Tanonga Nswana
Songwriter

Lyrics

Yeh
Lalala
You know sometimes I wonder
There are so many people that do good to us but we do not do good to them
Why is it like this
Yeh
Yabababababababa
Here a son
His mother really tries the best
To impress him so he could do better
Live a good life when he grows up later
Everything little money that she makes
She could give it to the son to invest
But there is nothing that the bwoy can makeup
Him waste all the money on women and drinkingup
Biggingup him friends but the bwoy has no future
Running up and down coz his life getting worser
His mother is crying
Bababababa
Mwati uziba ati nikukonda iwe
Bababababa
Mwati mwati umaziba mutima wanga uli pali weh
Eya eya
Mwati uziba ati nikukonda iwe
Yeh
Mwati mwati umaziba mutima wanga ulipali weh
Lalalala
Kuli Muzimai wina wapa neighbor
Mwamuna wake samu sunga bwino
Kuchokela chabe pamene banakwatilana
Ntawi zonse bango nkala chabe bayambana
Mwamuna wake pena samagona napanyumba
Chioneka alina mukazi kwina
Mukazi wake daily ango lila
Babababababa
Mwati uziba ati nikukonda iwe
Bababababa
Mwati mwati umaziba mutima wanga uli pali weh
Eya eya
Mwati uziba ati nikukonda iwe
Yeh
Mwati mwati umaziba mutima wanga ulipali weh
Lalalala
Kambili mulungu wamene anatilenga
Sitima nvelela vamene amakamba
Timafuna chabe nvelela satana
Nakuchita vintu vamene mutima umafuna
Kambili mulungu wamene anatilenga
Sitima nvelela vamene amakamba
Timafuna chabe nvelela satana
Nakuchita vintu vamene mutima umafuna
Kambili mulungu wamene anatilenga
Sitima nvelela vamene amakamba
Timafuna chabe nvelela satana
Nakuchita vintu vamene mutima umafuna
Mwati uziba ati nikukonda iwe
Bababababa
Mwati mwati umaziba mutima wanga uli pali weh
Eya eya
Mwati uziba ati nikukonda iwe
Yeh
Mwati mwati umaziba mutima wanga ulipali weh
Lalalala
Written by: Tanonga Nswana
instagramSharePathic_arrow_out